-
2 Samueli 14:7Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
7 Tsopano banja lonse landiukira ine mtumiki wanu ndipo aliyense akunena kuti, ‘Bweretsa wopha m’bale wakeyo+ kuti timuphe chifukwa cha moyo wa m’bale wake amene anamupha,+ ndipo tiwononge wolandira cholowayo!’ Tsopano anthuwa adzazimitsa makala anga onyeka otsalawo, kuti pasakhale wosunga dzina la mwamuna wanga kapena mbewu yake yotsala padziko lapansi.”+
-