Levitiko 15:2 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 2 “Lankhula ndi ana a Isiraeli kuti, ‘Mwamuna aliyense akakhala ndi nthenda ya kukha+ kumaliseche, nthenda yakeyo ndi yodetsedwa. Numeri 5:2 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 2 “Lamula ana a Isiraeli kuti azitulutsa mumsasa munthu aliyense wakhate,+ aliyense wakukha kumaliseche,+ ndi aliyense wodetsedwa chifukwa chokhudza mtembo wa munthu.+
2 “Lankhula ndi ana a Isiraeli kuti, ‘Mwamuna aliyense akakhala ndi nthenda ya kukha+ kumaliseche, nthenda yakeyo ndi yodetsedwa.
2 “Lamula ana a Isiraeli kuti azitulutsa mumsasa munthu aliyense wakhate,+ aliyense wakukha kumaliseche,+ ndi aliyense wodetsedwa chifukwa chokhudza mtembo wa munthu.+