Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 121:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  4 Taonani! Amene akuyang’anira Isiraeli,+

      Sangawodzere kapena kugona.+

  • Salimo 135:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Makutu ali nawo koma satha kumva.+

      Komanso m’mphuno mwawo mulibe mpweya.+

  • Yesaya 40:28
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 28 Kodi iwe sukudziwa kapena kodi sunamve?+ Yehova, Mlengi wa malekezero a dziko lapansi, ndiye Mulungu mpaka kalekale.+ Iye satopa kapena kufooka.+ Palibe amene angadziwe zimene iyeyo amazimvetsa.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena