Salimo 48:5 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 5 Iwo anaona ndipo anadabwa.Anasokonezeka, moti anathawa mopanikizika kwambiri.+ Miyambo 28:1 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 28 Anthu oipa amathawa popanda wowathamangitsa,+ koma olungama ali ngati mkango wamphamvu umene umakhala wolimba mtima.+
28 Anthu oipa amathawa popanda wowathamangitsa,+ koma olungama ali ngati mkango wamphamvu umene umakhala wolimba mtima.+