Luka 3:38 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 38 mwana wa Enosi,+mwana wa Seti,+mwana wa Adamu,+mwana wa Mulungu. 1 Akorinto 15:45 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 45 Zinachita kulembedwa kuti: “Munthu woyambirira, Adamu, anakhala munthu wamoyo.”+ Adamu womalizira anakhala mzimu+ wopatsa moyo.+
45 Zinachita kulembedwa kuti: “Munthu woyambirira, Adamu, anakhala munthu wamoyo.”+ Adamu womalizira anakhala mzimu+ wopatsa moyo.+