Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 50:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Kenako anafika pamalo opunthira mbewu+ a Atadi m’chigawo cha Yorodano.+ Kumeneko, anthuwo analira ndi kubuma kwakukulu, ndipo Yosefe anachita nawo miyambo yolirira maliro a bambo ake kwa masiku 7.+

  • 2 Samueli 3:35
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 35 Pambuyo pake, anthu onse anabwera kwa Davide tsiku lomwelo kudzam’patsa chakudya+ chomutonthoza, koma Davide analumbira kuti: “Mulungu andilange+ mowirikiza ngati ndidzalawa chakudya kapena kena kalikonse dzuwa lisanalowe!”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena