1 Mafumu 15:26 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 26 Iye anali kuchita zoipa+ pamaso pa Yehova, ndipo anapitiriza kutsatira njira ya bambo ake+ ndi machimo awo amene anachimwitsa nawo Isiraeli.+ 1 Mafumu 22:52 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 52 Iye anapitiriza kuchita zoipa+ pamaso pa Yehova. Anayenda m’njira ya bambo ake,+ m’njira ya mayi ake,+ ndiponso m’njira ya Yerobowamu+ mwana wa Nebati, amene anachimwitsa Isiraeli.+ 2 Mafumu 15:24 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 24 Iye anapitiriza kuchita zoipa pamaso pa Yehova.+ Sanasiye machimo a Yerobowamu+ mwana wa Nebati, amene anachimwitsa nawo Isiraeli.+
26 Iye anali kuchita zoipa+ pamaso pa Yehova, ndipo anapitiriza kutsatira njira ya bambo ake+ ndi machimo awo amene anachimwitsa nawo Isiraeli.+
52 Iye anapitiriza kuchita zoipa+ pamaso pa Yehova. Anayenda m’njira ya bambo ake,+ m’njira ya mayi ake,+ ndiponso m’njira ya Yerobowamu+ mwana wa Nebati, amene anachimwitsa Isiraeli.+
24 Iye anapitiriza kuchita zoipa pamaso pa Yehova.+ Sanasiye machimo a Yerobowamu+ mwana wa Nebati, amene anachimwitsa nawo Isiraeli.+