5 Usaziweramire kapena kuzitumikira,+ chifukwa ine Yehova Mulungu wako, ndine Mulungu wofuna kuti anthu azidzipereka kwa ine ndekha,*+ wolanga ana, zidzukulu ndi ana a zidzukuluzo, chifukwa cha zolakwa za abambo a anthu odana ndi ine.+
6 Koma inuyo ndi ana anu mukadzabwerera n’kusiya kunditsatira,+ osasunga malamulo anga amene ndakupatsani, komanso mukadzapita kukatumikira milungu ina+ ndi kuigwadira,