Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ezara 6:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Ndiyeno ana a Isiraeli, ansembe, Alevi+ ndi anthu ena onse amene anachokera ku ukapolo,+ anatsegulira+ nyumba ya Mulunguyo mosangalala.

  • Ezara 6:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Pamwambo wotsegulira nyumba ya Mulunguyo, anapereka nsembe ng’ombe zamphongo 100, nkhosa zamphongo 200, ndi ana a nkhosa amphongo 400. Anaperekanso mbuzi zamphongo 12 za nsembe ya machimo ya ana onse a Isiraeli mogwirizana ndi chiwerengero cha mafuko a Isiraeli.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena