Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ezara 6:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Ikhale ndi mizere itatu ya miyala yochita kuigubuduzira+ pamalopo ndi mzere umodzi wa matabwa.+ Ndalama zake zichokere kunyumba ya mfumu.+

  • Ezara 6:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Ineyo ndaika lamulo+ lokhudza zimene muyenera kuchita ndi akulu a Ayuda amenewa pa ntchito yomanganso nyumba ya Mulungu. Amuna amenewa muziwapatsa+ ndalama mosalekeza+ zochokera pa chuma cha mfumu+ zomwe anthu a kutsidya la Mtsinje amapereka pokhoma msonkho.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena