Ezara 8:19 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 19 Panalinso Hasabiya, yemwe anali pamodzi ndi Yesaiya wochokera pa ana a Merari,+ abale ake ndi ana awo. Onse pamodzi analipo 20. Nehemiya 12:21 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 21 Woimira nyumba ya Hilikiya anali Hasabiya ndipo woimira nyumba ya Yedaya+ anali Netaneli.
19 Panalinso Hasabiya, yemwe anali pamodzi ndi Yesaiya wochokera pa ana a Merari,+ abale ake ndi ana awo. Onse pamodzi analipo 20.