-
Esitere 1:22Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
22 Choncho mfumu inalemba makalata ndi kuwatumiza+ m’zigawo zonse za ufumu wake. Chigawo chilichonse+ anachilembera kalata malinga ndi mmene anthu a kumeneko amalembera ndiponso malinga ndi chinenero chawo. Anachita izi kuti mwamuna aliyense apitirize kutsogolera banja lake monga mutu,+ ndiponso kuti banjalo lizilankhula chinenero cha anthu a mtundu wa mwamunayo.
-