Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Deuteronomo 21:21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 Pamenepo amuna onse a mumzinda wawo azim’ponya miyala ndi kumupha. Muzichotsa woipayo pakati panu, ndipo Aisiraeli onse adzamva ndi kuchita mantha kwambiri.+

  • Esitere 9:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Pamenepo Esitere anati: “Ngati zingakukomereni mfumu,+ lolani kuti mawa Ayuda amene ali mu Susani achite mogwirizana ndi zimene lamulo laleroli likunena.+ Lolani kuti ana aamuna 10 a Hamani apachikidwe pamtengo.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena