Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 24:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  8 “Kodi Mfumu yaulemerero imeneyi ndani?”+

      “Ndi Yehova, wanyonga ndi wamphamvu,+

      Yehova wamphamvu mu nkhondo.”+

  • Salimo 99:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  4 Iye amakonda chilungamo ngati mmene mfumu yamphamvu imachitira.+

      Inu mwakhazikitsa kulungama.+

      Mwakhazikitsa chiweruzo ndi chilungamo pakati pa ana a Yakobo.+

  • Yeremiya 32:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Inu mumasonyeza anthu masauzande ambiri kukoma mtima kosatha.+ Mumabwezera zolakwa za abambo kwa ana awo.*+ Inu ndinu Mulungu woona, wamkulu+ ndi wamphamvu,+ ndipo dzina lanu+ ndinu Yehova wa makamu.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena