Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 13:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 “Ndiyeno m’tsogolo, mwana wanu akadzakufunsani+ kuti, ‘Kodi zimenezi zikutanthauza chiyani?’ Mudzamuyankhe kuti, ‘Yehova anatitulutsa ndi mphamvu ya dzanja lake mu Iguputo,+ m’nyumba ya ukapolo.+

  • Oweruza 6:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Ndiyeno Gidiyoni anayankha kuti: “Pepani mbuyanga, koma ngati Yehova ali ndi ife, n’chifukwa chiyani zonsezi zatigwera?+ Nanga ntchito zake zodabwitsa zija,+ zimene makolo athu anatisimbira zili kuti?+ Iwo anatiuza kuti, ‘Yehova ndiye anatitulutsa mu Iguputo.’+ Koma tsopano Yehova watisiya,+ ndipo watipereka m’manja mwa Amidiyani.”

  • Salimo 78:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  3 Amene tinamva ndipo tikuwadziwa,+

      Komanso amene makolo athu anatifotokozera.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena