Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yeremiya 11:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Yehova wakutchulani dzina+ lakuti, ‘Mtengo waukulu wa maolivi wa masamba ambiri obiriwira, wokongola, wobala zipatso komanso wooneka bwino.’ Koma pali phokoso lamphamvu ndipo mtengowo auyatsa moto, komanso adani athyola nthambi zake.+

  • Hoseya 14:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 Nthambi zake zidzaphukira ndipo adzakhala ndi ulemerero ngati mtengo wa maolivi.+ Fungo lake lonunkhira lidzakhala ngati mtengo wa ku Lebanoni.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena