Salimo 119:8 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 8 Ndikupitiriza kusunga malangizo anu,+Choncho musandisiyiretu.+ Salimo 119:93 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 93 Sindidzaiwala malamulo anu mpaka kalekale,+Chifukwa mwandisungabe wamoyo kudzera m’malamulo amenewo.+
93 Sindidzaiwala malamulo anu mpaka kalekale,+Chifukwa mwandisungabe wamoyo kudzera m’malamulo amenewo.+