Mateyu 6:11 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 11 Mutipatse ife lero chakudya chathu chalero.+ 1 Timoteyo 6:8 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 8 Choncho, pokhala ndi chakudya, zovala ndi pogona, tikhale okhutira ndi zinthu zimenezi.+