Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 119:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  6 Pamenepo sindikanachita manyazi,+

      Pamene ndikulabadira malamulo anu onse.+

  • Aroma 13:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Pakuti olamulira amaopsa ngati ukuchita zoipa,+ osati ngati ukuchita zabwino. Choncho kodi ukufuna kuti usamachite mantha ndi olamulira? Pitiriza kuchita zabwino,+ ndipo olamulira adzakutamanda.

  • Aroma 13:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Chotero pali chifukwa chabwino chakuti anthu inu mukhalire ogonjera, osati chabe chifukwa choopa mkwiyo umenewo, komanso chifukwa cha chikumbumtima chanu.+

  • 1 Petulo 3:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Ndithudi, ndani angakuchitireni zoipa mukakhala odzipereka pochita zabwino?+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena