Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 99:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  4 Iye amakonda chilungamo ngati mmene mfumu yamphamvu imachitira.+

      Inu mwakhazikitsa kulungama.+

      Mwakhazikitsa chiweruzo ndi chilungamo pakati pa ana a Yakobo.+

  • Yeremiya 10:24
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 24 Ndikonzeni, inu Yehova. Koma mundikonze ndi chiweruzo chanu+ osati mutakwiya+ chifukwa mungandifafanize.+

  • Aroma 2:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Tikudziwa kuti Mulungu amaweruza anthu amene amachita zimenezi kuti ndi oyenera kulandira chilango ndipo chiweruzo chake ndi chogwirizana ndi choonadi.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena