Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 89:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Pa nthawi imeneyo munalankhula ndi okhulupirika anu mwa masomphenya,+

      Ndipo munati:

      “Ndapereka thandizo kwa wamphamvu.+

      Ndakweza wosankhidwa mwapadera pakati pa anthu.+

  • Luka 9:35
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 35 Ndiyeno mawu+ anatuluka mumtambomo akuti: “Uyu ndiye Mwana wanga, amene ndinam’sankha.+ Mumvereni.”+

  • 1 Petulo 2:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Pamene mukubwera kwa iye, amene ndiye mwala wamoyo+ umene anthu+ anaukana,+ koma umene Mulungu anausankha, umenenso uli wamtengo wapatali kwa iye,+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena