17 Iwo adzakuimbira nyimbo yoimba polira.+ Azidzati:
“‘“Iwe mzinda wotamandika, zoona wawonongekadi! Mwa iwe munali kukhala anthu ochokera kunyanja.+ Unali wamphamvu panyanja.+ Iwe ndi anthu ako munali kuchititsa mantha anthu onse okhala padziko lapansi.