Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yesaya 54:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 “Kwa kanthawi kochepa ndinakusiyiratu,+ koma ndidzakusonkhanitsa pamodzi mwachifundo chachikulu.+

  • Ezekieli 37:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 Ndidzakuikirani mitsempha ndi kukupatsani mnofu. Ndidzakukutani ndi khungu ndi kuika mpweya mwa inu ndipo mudzakhala ndi moyo.+ Choncho mudzadziwa kuti ine ndine Yehova.”’”+

  • Hagai 2:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 “‘Ulemerero wa nyumba yatsopanoyi udzakhala waukulu kuposa wa nyumba yoyamba ija,’+ watero Yehova wa makamu.

      “‘Ndipo ndidzakhazikitsa mtendere pamalo awa,’+ watero Yehova wa makamu.”

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena