Ekisodo 6:8 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 8 Ine ndidzakulowetsani m’dziko limene ndinalumbirira+ Abulahamu, Isaki ndi Yakobo, nditakweza dzanja langa. Ndidzakupatsani dzikolo kukhala lanu.+ Ine ndine Yehova.’”+ Deuteronomo 32:40 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 40 Ndikukweza dzanja langa kumwamba polumbira,+Ndipo ndikunena kuti: “Pali ine, Mulungu wamoyo wosatha,”+ Ezekieli 47:14 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 14 Anthu inu muyenera kutenga dziko limeneli monga cholowa chanu. Inetu ndinalumbira nditakweza dzanja+ kuti ndidzapereka dziko limeneli kwa makolo anu.+ Choncho mugawane dzikoli mwa kuchita maere kuti likhale cholowa chanu. Aliyense alandire gawo lofanana ndi la m’bale wake.+
8 Ine ndidzakulowetsani m’dziko limene ndinalumbirira+ Abulahamu, Isaki ndi Yakobo, nditakweza dzanja langa. Ndidzakupatsani dzikolo kukhala lanu.+ Ine ndine Yehova.’”+
40 Ndikukweza dzanja langa kumwamba polumbira,+Ndipo ndikunena kuti: “Pali ine, Mulungu wamoyo wosatha,”+
14 Anthu inu muyenera kutenga dziko limeneli monga cholowa chanu. Inetu ndinalumbira nditakweza dzanja+ kuti ndidzapereka dziko limeneli kwa makolo anu.+ Choncho mugawane dzikoli mwa kuchita maere kuti likhale cholowa chanu. Aliyense alandire gawo lofanana ndi la m’bale wake.+