Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Nehemiya 1:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 1 Awa ndi mawu a Nehemiya+ mwana wa Hakaliya. M’mwezi wa Kisilevi,*+ m’chaka cha 20,+ ine ndinali kunyumba ya mfumu yokhala ndi mpanda wolimba kwambiri ya ku Susani.+

  • Esitere 2:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Ndiyeno mawu a mfumu ndi malamulo ake atamveka, komanso atsikana ambiri atawasonkhanitsa pamodzi kunyumba ya mfumu yokhala ndi mpanda wolimba kwambiri ya ku Susani+ kuti Hegai+ aziwayang’anira, Esitere nayenso anam’tengera kunyumba ya mfumu komweko kuti Hegai woyang’anira akazi azimuyang’anira.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena