Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Mafumu 23:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Mfumuyo inachotsa ntchito ansembe a milungu yachilendo, amene mafumu a Yuda anawaika kuti azifukiza nsembe yautsi pamalo okwezeka m’mizinda ya Yuda ndi malo ozungulira Yerusalemu. Inachotsanso ntchito ansembe ofukiza nsembe yautsi kwa Baala,+ kwa dzuwa, kwa mwezi, kwa magulu a nyenyezi, ndi kwa khamu lonse la zinthu zakuthambo.+

  • Hoseya 10:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Anthu okhala ku Samariya adzachita mantha ndi fano la ku Beti-aveni+ la mwana wa ng’ombe. Pakuti anthuwo pamodzi ndi ansembe a mulungu wachilendo, amene anali kusangalala ndi fanolo chifukwa cha ulemerero wake, adzalilirira. Adzalirira fanolo chifukwa ulemerero wake udzachoka likadzatengedwa kupita kudziko lina.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena