Maliko 15:31 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 31 Chimodzimodzinso ansembe aakulu. Nawonso anali kumuchita chipongwe limodzi ndi alembi. Iwo anali kunena kuti: “Ena anatha kuwapulumutsa, koma kuti adzipulumutse yekha zikum’kanika!+ Luka 23:35 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 35 Anthu anangoima chilili kuonerera zochitikazo.+ Koma olamulira anali kumunyogodola kuti: “Ena anatha kuwapulumutsa, m’lekeni adzipulumutse yekha,+ ngati iyeyu alidi Khristu wa Mulungu, Wosankhidwa.”+
31 Chimodzimodzinso ansembe aakulu. Nawonso anali kumuchita chipongwe limodzi ndi alembi. Iwo anali kunena kuti: “Ena anatha kuwapulumutsa, koma kuti adzipulumutse yekha zikum’kanika!+
35 Anthu anangoima chilili kuonerera zochitikazo.+ Koma olamulira anali kumunyogodola kuti: “Ena anatha kuwapulumutsa, m’lekeni adzipulumutse yekha,+ ngati iyeyu alidi Khristu wa Mulungu, Wosankhidwa.”+