Mateyu 24:5 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 5 chifukwa ambiri adzabwera m’dzina langa ndi kunena kuti, ‘Khristu uja ndine,’ ndipo adzasocheretsa anthu ambiri.+ Maliko 13:6 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 6 Ambiri adzabwera m’dzina langa, ndi kunena kuti, ‘Khristu uja ndine,’ ndipo adzasocheretsa anthu ambiri.+
5 chifukwa ambiri adzabwera m’dzina langa ndi kunena kuti, ‘Khristu uja ndine,’ ndipo adzasocheretsa anthu ambiri.+
6 Ambiri adzabwera m’dzina langa, ndi kunena kuti, ‘Khristu uja ndine,’ ndipo adzasocheretsa anthu ambiri.+