Machitidwe 9:2 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 2 kukamupempha zikalata za chilolezo zopita nazo kumasunagoge a ku Damasiko. Anapempha zikalatazo kuti akakapeza wina aliyense wotsatira Njirayo,*+ mwamuna kapena mkazi, akabwere naye ku Yerusalemu ali womangidwa. Machitidwe 9:14 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 14 Ndipo panopo ansembe aakulu amupatsa mphamvu kuti amange onse oitana pa dzina lanu.”+
2 kukamupempha zikalata za chilolezo zopita nazo kumasunagoge a ku Damasiko. Anapempha zikalatazo kuti akakapeza wina aliyense wotsatira Njirayo,*+ mwamuna kapena mkazi, akabwere naye ku Yerusalemu ali womangidwa.