Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 3:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Atatero maso awo anatseguka, ndipo anazindikira kuti ali maliseche.+ Choncho anadzisokera masamba a mkuyu n’kupanga zovala zomangira m’chiuno.+

  • Genesis 3:21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 Kenako Yehova Mulungu anapangira Adamu ndi mkazi wake zovala zazitali zachikopa, n’kuwaveka.+

  • 2 Timoteyo 2:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 M’nyumba yaikulu simukhala ziwiya zagolide ndi zasiliva zokha ayi, koma mumakhalanso zamtengo ndi zadothi. Ziwiya zina zimakhala za ntchito yolemekezeka koma zina zimakhala za ntchito yonyozeka.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena