Aheberi 8:6 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 6 Koma tsopano Yesu walandira ntchito yapamwamba kwambiri yotumikira ena, moti wakhalanso mkhalapakati+ wa pangano labwino kwambiri,+ limene lakhazikitsidwa mwalamulo pa malonjezo abwinonso.+ 1 Yohane 2:20 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 20 Inu munadzozedwa ndi woyerayo,+ ndipo nonsenu ndinu odziwa choonadi.+
6 Koma tsopano Yesu walandira ntchito yapamwamba kwambiri yotumikira ena, moti wakhalanso mkhalapakati+ wa pangano labwino kwambiri,+ limene lakhazikitsidwa mwalamulo pa malonjezo abwinonso.+