1 Akorinto 1:4 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 4 Nthawi zonse ndimayamika Mulungu chifukwa cha inu, poona kukoma mtima kwakukulu+ kwa Mulungu kumene anakusonyezani kudzera mwa Khristu Yesu,+ Afilipi 1:3 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 3 Ndimayamika Mulungu wanga nthawi zonse ndikakumbukira za inu.+
4 Nthawi zonse ndimayamika Mulungu chifukwa cha inu, poona kukoma mtima kwakukulu+ kwa Mulungu kumene anakusonyezani kudzera mwa Khristu Yesu,+