Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Deuteronomo 31:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Sonkhanitsani anthu,+ amuna, akazi, ana ndi alendo okhala m’mizinda yanu, kuti amvetsere ndi kuphunzira,+ pakuti ayenera kuopa Yehova Mulungu wanu+ ndi kutsatira mosamala mawu onse a m’chilamulo ichi.

  • Mateyu 18:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Pakuti kulikonse kumene awiri kapena atatu asonkhana m’dzina langa,+ ine ndidzakhala pakati pawo.”+

  • Machitidwe 2:42
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 42 Chotero iwo anapitiriza kulabadira zimene atumwiwo anali kuphunzitsa. Iwo anali kugawana zinthu,+ kudya chakudya+ komanso kupemphera.+

  • Machitidwe 20:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 M’chipinda cham’mwamba+ mmene tinasonkhanamo, munali nyale zambiri ndithu.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena