Yohane 4:36 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 36 wokolola akulandira kale malipiro ndipo akusonkhanitsa zipatso ku moyo wosatha,+ kuti wofesa mbewu+ ndi wokolola asangalalire pamodzi.+ Aheberi 10:35 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 35 Chotero, musataye ufulu wanu wa kulankhula,+ umene udzabweretse mphoto yaikulu kwambiri.+
36 wokolola akulandira kale malipiro ndipo akusonkhanitsa zipatso ku moyo wosatha,+ kuti wofesa mbewu+ ndi wokolola asangalalire pamodzi.+