Yesaya 38:10 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 10 Ine ndinati: “Pakatikati pa masiku anga ndidzalowa pazipata+ za Manda.Ndidzamanidwa zaka zanga zotsala.”+ Mateyu 16:18 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 18 Chotero inenso ndikukuuza kuti, Iwe ndiwe Petulo,+ ndipo pathanthwe+ ili ndidzamangapo mpingo wanga. Zipata za Manda+ sizidzaugonjetsa.+ Yohane 6:54 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 54 Wakudya mnofu wanga ndi kumwa magazi anga ali nawo moyo wosatha, ndipo ndidzamuukitsa+ kwa akufa tsiku lomaliza. Yohane 11:25 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 25 Pamenepo Yesu anati: “Ine ndine kuuka ndi moyo.+ Aliyense wokhulupirira mwa ine, ngakhale amwalire, adzakhalanso ndi moyo.+
10 Ine ndinati: “Pakatikati pa masiku anga ndidzalowa pazipata+ za Manda.Ndidzamanidwa zaka zanga zotsala.”+
18 Chotero inenso ndikukuuza kuti, Iwe ndiwe Petulo,+ ndipo pathanthwe+ ili ndidzamangapo mpingo wanga. Zipata za Manda+ sizidzaugonjetsa.+
54 Wakudya mnofu wanga ndi kumwa magazi anga ali nawo moyo wosatha, ndipo ndidzamuukitsa+ kwa akufa tsiku lomaliza.
25 Pamenepo Yesu anati: “Ine ndine kuuka ndi moyo.+ Aliyense wokhulupirira mwa ine, ngakhale amwalire, adzakhalanso ndi moyo.+