Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 41:5-7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Ndiyeno Farao anagonanso nʼkulota maloto ena. Mʼmalotowa anaona ngala za tirigu 7 zikutuluka paphesi limodzi. Ngalazo zinali zokhwima ndi zazikulu bwino.+ 6 Pambuyo pake anaonanso ngala zina 7 zikutuluka. Ngalazo zinali zonyala komanso zowauka ndi mphepo yakumʼmawa. 7 Ngala zonyalazo zinayamba kumeza ngala 7 zokhwima ndi zazikulu bwinozo. Kenako Farao anadzidzimuka ndipo anazindikira kuti anali maloto.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena