Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 37:27
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 27 Tiyeni timugulitse+ kwa Aisimaeliwa, tisamuvulaze. Ndipotu ndi mʼbale wathu ameneyu, magazi amodzi.”* Choncho iwo anamvera zimene mʼbale wawoyo ananena.

  • Genesis 37:35
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 35 Ana ake onse aamuna ndi aakazi ankapita kukamutonthoza, koma iye ankakana kutonthozedwa. Ankanena kuti: “Ayi! Ndidzalira mpaka kutsikira ku Manda*+ kumene kuli mwana wanga.” Ndipo bambo akewo anapitiriza kumulira.

  • Genesis 44:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Ife tinakuyankhani mbuyanga kuti, ‘Bambo tili nawo koma ndi okalamba. Ali ndi mwana amene anabereka atakalamba, yemwe ndi wamngʼono kwa tonsefe.+ Mʼbale wake wa mimba imodzi anamwalira,+ moti anatsala yekha+ ndipo bambo amamukonda kwambiri.’

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena