Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 41:30
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 30 Koma pambuyo pa zaka zimenezo, padzabwera zaka 7 za njala. Chakudya chonse chochuluka cha mʼdziko la Iguputo chija chidzaiwalika, ndipo njalayo idzawononga dziko lonse.+

  • Genesis 47:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Chakacho chitatha, anthu anayamba kupita kwa iye chaka chotsatira. Iwo ankanena kuti: “Tisakubisireni mbuyathu, ndalama zathu ndi ziweto zonse zatha chifukwa tinazipereka kwa inu. Tilibenso chilichonse choti tikupatseni kupatulapo matupi athuwa komanso minda yathu.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena