Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Deuteronomo 32:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  4 Iye ndi Thanthwe, ndipo ntchito yake ndi yangwiro,+

      Njira zake zonse ndi zolungama.+

      Mulungu wokhulupirika,+ amene sachita zinthu zopanda chilungamo.+

      Iye ndi wolungama ndi wowongoka.+

  • Salimo 104:24
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 24 Ntchito zanu ndi zochuluka, inu Yehova!+

      Zonsezo munazipanga mwanzeru.+

      Dziko lapansi ladzaza ndi zinthu zimene munapanga.

  • 1 Timoteyo 4:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Chifukwa chilichonse cholengedwa ndi Mulungu nʼchabwino,+ ndipo palibe chimene chiyenera kukanidwa+ ngati munthu wayamika Mulungu pakudya,

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena