Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 32:13-15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Tsiku limenelo Yakobo anagona pamalopo. Kenako anatenga zinthu zina pa chuma chake kuti akapatse mchimwene wake Esau ngati mphatso.+ 14 Anatenga mbuzi zazikazi 200, mbuzi zamphongo 20, nkhosa zazikazi 200, nkhosa zamphongo 20, 15 ngamila zoyamwitsa 30 ndi ana a ngamilazo, ngʼombe zazikazi 40, ngʼombe zamphongo 10, abulu aakazi 20 ndi abulu amphongo 10.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena