Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Deuteronomo 32:11, 12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Monga mmene chiwombankhanga chimagwedezera chisa chake,

      Mmene chimaulukira pamwamba pa ana ake,

      Mmene chimatambasulira mapiko ake, kuti chitenge anawo,

      Nʼkuwanyamula pamapiko ake,+

      12 Ndi Yehova yekha amene anapitiriza kumutsogolera,*+

      Panalibe mulungu wachilendo amene anali naye.+

  • Yesaya 63:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  9 Pa nthawi yonse imene iwo ankavutika, iye ankavutikanso.+

      Ndipo mthenga wake* anawapulumutsa.+

      Iye anawawombola chifukwa cha chikondi komanso chifundo chake,+

      Ndipo nthawi zonse ankawakweza mʼmwamba komanso kuwanyamula.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena