Levitiko 23:6 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 6 Pa tsiku la 15 la mwezi umenewu, muzichitira Yehova Chikondwerero cha Mikate Yopanda Zofufumitsa.+ Muzidya mikate yopanda zofufumitsa kwa masiku 7.+ Luka 22:7 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 7 Tsopano tsiku la Chikondwerero cha Mikate Yopanda Zofufumitsa linafika, tsiku limene nsembe ya Pasika inkayenera kuperekedwa.+
6 Pa tsiku la 15 la mwezi umenewu, muzichitira Yehova Chikondwerero cha Mikate Yopanda Zofufumitsa.+ Muzidya mikate yopanda zofufumitsa kwa masiku 7.+
7 Tsopano tsiku la Chikondwerero cha Mikate Yopanda Zofufumitsa linafika, tsiku limene nsembe ya Pasika inkayenera kuperekedwa.+