Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 36:14-18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Ndiyeno anapanga nsalu za ubweya wa mbuzi zoyala pachihema. Anapanga nsalu 11.+ 15 Nsalu iliyonse inali mamita 13 mulitali ndipo mulifupi inali mamita awiri. Nsalu zonse 11 muyezo wake unali wofanana. 16 Kenako analumikiza nsalu 5 pamodzi komanso analumikiza nsalu zina 6 pamodzi. 17 Atatero anaika zingwe zopota 50 zokolekamo ngowe mʼmphepete mwa nsalu yakumapeto kwenikweni, polumikizirana nsalu ziwirizi. Anaikanso zingwe zopota 50 zokolekamo ngowe mʼmphepete mwa nsalu inayo, pamalo amene nsalu ziwirizi zinalumikizana. 18 Atatero anapanga ngowe 50 zakopa zolumikizira nsaluzo kuti zikhale chinsalu chimodzi.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena