Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 36:27-30
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 27 Anapanga mafelemu 6 nʼkuwaika kumbuyo kwa chihemacho, mbali yakumadzulo.+ 28 Anapanga mafelemu awiri kuti akhale ochirikiza mʼmakona awiri akumbuyo kwa chihemacho. 29 Mafelemu amenewo anali ndi matabwa awiri ophatikiza kuyambira pansi mpaka pamwamba, pamene pali mphete yoyamba. Izi nʼzimene anachita ndi mafelemu onse ochirikiza mʼmakona. 30 Choncho anapanga mafelemu 8 ndi zitsulo 16 zasiliva zokhazikapo mafelemuwo. Zitsulo ziwiri zinali pansi pa felemu lililonse.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena