Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 38:18, 19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Nsalu yotchinga pakhomo la bwalo anaiwomba ndi ulusi wabuluu, ubweya wa nkhosa wapepo, ulusi wofiira kwambiri ndi ulusi wopota wabwino kwambiri. Inali mamita 9 mulitali mwake, ndipo kutalika kwake kuchokera pansi mpaka mʼmwamba inali mamita awiri, mofanana ndi nsalu zotchingira mpanda wa bwalo.+ 19 Zipilala zake 4 ndi zitsulo 4 zokhazikapo zipilalazo zinali zakopa. Tizitsulo ta zipilalazo tokolowekapo nsalu tinali tasiliva, ndipo pamwamba pa zipilalazo ndi tizitsulo tolumikizira anazikuta ndi siliva.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena