Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Levitiko 3:9, 10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Ndipo pansembe yamgwirizanoyo azitengapo mafuta ake ndi kuwapereka kwa Yehova+ monga nsembe yowotcha pamoto. Azichotsa mchira wonse wamafuta pafupi ndi fupa la msana ndiponso mafuta okuta matumbo ndi mafuta onse amene ali pamatumbo. 10 Azichotsanso impso ziwiri zomwe zili pafupi ndi chiuno ndi mafuta okuta impsozo. Komanso azichotsa mafuta apachiwindi pamodzi ndi impsozo.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena