22 Ndiyeno ndinauza Alevi kuti azidziyeretsa nthawi zonse komanso azibwera kudzalondera mageti a mzinda kuti tsiku la Sabata likhale loyera.+ Inu Mulungu wanga, mundikumbukirenso pa zimenezi ndipo mundichitire chifundo mogwirizana ndi kuchuluka kwa chikondi chanu chokhulupirika.+