Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Numeri 14:35
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 35 Ine Yehova ndalankhula. Zimene ndidzachitire gulu lonse la anthu oipali, amene asonkhana kuti atsutsane ndi ine ndi izi: Onse adzafera mʼchipululu muno ndipo adzathera momwe muno.+

  • Numeri 16:1, 2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Kenako Kora+ mwana wa Izara,+ mwana wa Kohati,+ mwana wa Levi,+ anagwirizana ndi adzukulu a Rubeni,+ omwe ndi Datani ndi Abiramu ana a Eliyabu,+ komanso Oni mwana wa Pelete, kuti aukire. 2 Iwo limodzi ndi amuna a Chiisiraeli okwana 250 anaukira Mose. Amunawa anali atsogoleri a anthuwo, amuna osankhidwa pakati pa Aisiraeli, amuna otchuka.

  • Numeri 16:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Kora atasonkhanitsa anthu onse omutsatira+ kuti atsutsane nawo pakhomo la chihema chokumanako, ulemerero wa Yehova unaonekera ku gulu lonselo.+

  • Numeri 16:35
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 35 Kenako moto unachokera kwa Yehova+ ndipo unapsereza amuna 250 omwe ankapereka nsembe zofukiza aja.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena