Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 18:15, 16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Mose anayankha apongozi akewo kuti: “Chifukwa anthuwa akumabwera kwa ine kuti adzamve malangizo a Mulungu. 16 Akakhala ndi mlandu pakati pawo akumabwera nawo kwa ine, ndipo ndikumaweruza nʼkuwauza chigamulo cha Mulungu woona ndi malamulo ake.”+

  • Ekisodo 33:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Yehova ankalankhula ndi Mose pamasomʼpamaso,+ mmene munthu amalankhulira ndi munthu mnzake. Mose akabwerera kumsasa, mtumiki wake Yoswa,+ mwana wa Nuni, sankachoka kuchihemako.

  • Levitiko 24:11, 12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Mnyamatayo anayamba kunyoza* ndi kutukwana dzina la Mulungu.*+ Ndiye anapita naye kwa Mose.+ Dzina la mayi ake linali Selomiti, mwana wa Dibiri wa fuko la Dani. 12 Ndiyeno anamutsekera kudikira kuti Yehova apereke chigamulo pa nkhaniyo.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena