Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Levitiko 23:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Muziwerenga masiku 50+ kukafika pa tsiku lotsatizana ndi tsiku limene Sabata la 7 lathera, kenako muzipereka nsembe yambewu zatsopano kwa Yehova.+

  • Levitiko 23:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Popereka mitanda ya mkateyi muziperekanso ana a nkhosa amphongo opanda chilema okwana 7, aliyense wa chaka chimodzi, komanso ngʼombe imodzi yaingʼono yamphongo ndi nkhosa ziwiri zamphongo.+ Zimenezi ziziperekedwa monga nsembe yopsereza, nsembe yowotcha pamoto yoperekedwa kwa Yehova. Ziziperekedwa pamodzi ndi nsembe yambewu ndi nsembe zachakumwa kuti zikhale kafungo kosangalatsa* kwa Yehova.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena